-
Levitiko 24:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Aroni azikhazika nyale pamalo ake, kunja kwa nsalu yotchinga ya Umboni m’chihema chokumanako. Nyaleyo iziunikira pamaso pa Yehova nthawi zonse kuyambira madzulo mpaka m’mawa. Limeneli ndi lamulo kwa inu mpaka kalekale m’mibadwo yanu yonse.
-