Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 38:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kumbali imodzi ya chipata cha bwalo, mpanda wa nsaluwo unali mikono 15. Kunali nsanamira zitatu ndi zitsulo zitatu zokhazikapo nsanamirazo.+

  • Ekisodo 39:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Anabweretsanso nsalu zotchingira+ bwalo, mizati+ ndi zitsulo zokhazikapo mizatiyo,+ nsalu yotchinga+ pachipata cha bwalo, zikhomo za bwalo+ ndi zingwe zogwira mpanda,+ ziwiya zonse+ zogwiritsa ntchito pa utumiki wa pachihema chopatulika, kapena kuti chihema chokumanako,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena