Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 30:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Aroni azifukiza zofukiza zonunkhira paguwapo.+ M’mawa uliwonse akamasamalira nyale,+ azifukiza zofukizazo.

  • Ekisodo 39:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 guwa lansembe+ lagolide, mafuta odzozera,+ zofukiza zonunkhira,+ nsalu yotchinga+ pakhomo la chihemacho,

  • Salimo 141:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pemphero langa likhale lokonzedwa ngati zofukiza+ pamaso panu,+

      Mapembedzero anga akhale ngati nsembe yambewu yamadzulo.+

  • Luka 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Khamu lonse la anthu linali kupemphera panja, pa ola lopereka nsembe zofukizalo.+

  • Chivumbulutso 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mngelo wina anafika ndi kuimirira kuguwa+ lansembe. Iye anali ndi chiwiya chofukiziramo chagolide, ndipo anamupatsa zofukiza zambiri+ kuti azipereke nsembe limodzi ndi mapemphero a oyera onse paguwa lansembe lagolide, limene linali pamaso pa mpando wachifumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena