Ekisodo 8:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Farao ataona kuti mliri wa achulewo watha, anaumitsa mtima wake,+ ndipo sanamvere Mose ndi Aroni, monga momwe Yehova ananenera.+ Ekisodo 8:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Pamenepo Mose anati: “Mmene ndikuchoka pano, ndikukachonderera Yehova ndipo mawa tizilomboti tichoka pa Farao, atumiki ake ndi anthu ake. Koma Farao asatipusitsenso mwa kusalola anthu kupita kuti akapereke nsembe kwa Yehova.”+ Ekisodo 10:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Zitatero anabweretsanso Mose ndi Aroni kwa Farao ndipo iye anati: “Pitani, katumikireni Yehova Mulungu wanu.+ Ndani kwenikweni amene akupita?” Ekisodo 12:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Nthawi yomweyo Farao anaitanitsa+ Mose ndi Aroni usiku, ndipo anati: “Nyamukani, chokani pakati pa anthu anga, inuyo ndi ana onse a Isiraeli. Pitani, katumikireni Yehova, monga momwe mwanenera.+
15 Farao ataona kuti mliri wa achulewo watha, anaumitsa mtima wake,+ ndipo sanamvere Mose ndi Aroni, monga momwe Yehova ananenera.+
29 Pamenepo Mose anati: “Mmene ndikuchoka pano, ndikukachonderera Yehova ndipo mawa tizilomboti tichoka pa Farao, atumiki ake ndi anthu ake. Koma Farao asatipusitsenso mwa kusalola anthu kupita kuti akapereke nsembe kwa Yehova.”+
8 Zitatero anabweretsanso Mose ndi Aroni kwa Farao ndipo iye anati: “Pitani, katumikireni Yehova Mulungu wanu.+ Ndani kwenikweni amene akupita?”
31 Nthawi yomweyo Farao anaitanitsa+ Mose ndi Aroni usiku, ndipo anati: “Nyamukani, chokani pakati pa anthu anga, inuyo ndi ana onse a Isiraeli. Pitani, katumikireni Yehova, monga momwe mwanenera.+