Ekisodo 3:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ndidzatambasula dzanja langa+ ndi kukantha Iguputo ndi ntchito zanga zonse zodabwitsa zimene ndidzazichita m’dzikolo. Pamenepo adzakulolani kuchoka.+ Ekisodo 6:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno Yehova anauza Mose kuti: “Tsopano uona zimene ndichite kwa Farao.+ Chifukwa cha dzanja lamphamvu, iye awalola kuchoka, ndipo chifukwa cha dzanja lamphamvu awatulutsa m’dziko lake.”+ Ekisodo 10:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Pamenepo Mose anati: “Tipita ndi achinyamata athu ndi achikulire omwe. Tipita ndi ana athu aamuna ndi ana athu aakazi+ pamodzi ndi nkhosa ndi ng’ombe zathu,+ chifukwa tikukachitira Yehova chikondwerero.”+ Salimo 105:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Aiguputo anasangalala pamene Aisiraeli anatuluka m’dzikolo,Pakuti anali kuwaopa kwambiri.+
20 Ndidzatambasula dzanja langa+ ndi kukantha Iguputo ndi ntchito zanga zonse zodabwitsa zimene ndidzazichita m’dzikolo. Pamenepo adzakulolani kuchoka.+
6 Ndiyeno Yehova anauza Mose kuti: “Tsopano uona zimene ndichite kwa Farao.+ Chifukwa cha dzanja lamphamvu, iye awalola kuchoka, ndipo chifukwa cha dzanja lamphamvu awatulutsa m’dziko lake.”+
9 Pamenepo Mose anati: “Tipita ndi achinyamata athu ndi achikulire omwe. Tipita ndi ana athu aamuna ndi ana athu aakazi+ pamodzi ndi nkhosa ndi ng’ombe zathu,+ chifukwa tikukachitira Yehova chikondwerero.”+