Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 13:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno pa tsiku limenelo udzauze mwana wako kuti, ‘Ndikuchita izi chifukwa cha zimene Yehova anandichitira potuluka mu Iguputo.’+

  • Deuteronomo 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Koma khalani tcheru ndipo musamale moyo wanu,+ kuti musaiwale zinthu zimene maso anu anaona,+ ndi kuti mitima yanu isaiwale zinthu zimenezo masiku onse a moyo wanu.+ Ana anu ndi zidzukulu zanu muziwauza za zinthu zimenezo,+

  • Deuteronomo 6:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pamenepo mwana wakoyo udzamuyankhe kuti, ‘Tinakhala akapolo a Farao ku Iguputo, koma Yehova anatitulutsa ku Iguputoko ndi dzanja lamphamvu.+

  • Salimo 44:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Inu Mulungu, ife tamva ndi makutu athu,

      Makolo athu anatifotokozera+

      Ntchito zimene inu munachita m’masiku awo,+

      M’masiku akale.+

  • Salimo 78:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu anaika chikumbutso pakati pa ana a Yakobo,+

      Iye anaika chilamulo mu Isiraeli,+

      Zinthu zimene analamula makolo athu,+

      Kuti auze ana awo.+

  • Yoweli 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Fotokozerani ana anu za zinthu zimenezi. Ana anu adzafotokozere ana awo, ndipo ana a ana anuwo adzafotokozerenso m’badwo wotsatira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena