Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 26:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zitatero, nthaka inayasama n’kuwameza.+ Koma Kora anafa pamene moto unanyeketsa gulu la amuna 250.+ Choncho iwowa anakhala chitsanzo chopereka chenjezo.+

  • Deuteronomo 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 kapena zimene anachitira Datani ndi Abiramu,+ ana a Eliyabu, mwana wa Rubeni, pamene dziko linatsegula pakamwa pake ndi kuwameza pamodzi ndi mabanja awo, mahema awo, ndi chamoyo china chilichonse chimene chinali pakati pawo. Dziko linawameza ali pakati pa Aisiraeli onse).+

  • Salimo 106:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo dziko lapansi linatseguka ndipo linameza Datani,+

      Ndi kufotsera msonkhano wa Abiramu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena