Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 34:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Lamula ana a Isiraeli, uwauze kuti, ‘Pamene mukukalowa m’dziko la Kanani,+ nawa malire a dziko+ limene mudzalandire ngati cholowa chanu.+

  • Yoswa 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Pitani mumsasa wonsewu, mukauze anthu kuti, ‘Konzekani ndi kutenga zonse zofunikira, chifukwa pakapita masiku atatu kuchokera lero, mudzawoloka Yorodano uyu, ndi kulowa m’dzikolo kuti mukalilande, dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti likhale lanu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena