Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 24:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Munthuyo atamva zimenezo, anapita n’kukalowa m’nyumbamo. Pamenepo Labani anamasula ngamila ndi kuzipatsa chakudya. Anatenganso madzi n’kusambitsa mapazi a mlendoyo ndi mapazi a anyamata omwe iye anali nawo.+

  • Genesis 43:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano munthuyo analowetsa amunawo m’nyumba ya Yosefe. Anawapatsa madzi kuti asambe mapazi awo,+ n’kuwapatsanso chakudya choti adyetse abulu awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena