Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Anawalamula kuti: “Inu mukabisale+ kumbuyo kwa mzindawo. Musakakhale patali kwambiri ndi mzindawo, ndipo nonsenu mukakhale okonzeka.

  • 1 Samueli 15:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako, Sauli anafika kumzinda wa Amaleki ndi kuubisalira kuchigwa.*

  • Miyambo 24:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iweyo udzatha kumenya nkhondo yako potsatira malangizo anzeru,+ ndipo pakakhala aphungu ochuluka anthu amapulumuka.+

  • Mlaliki 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndi bwino kukhala ndi nzeru kuposa kukhala ndi zida zomenyera nkhondo, ndipo wochimwa mmodzi yekha akhoza kuwononga zabwino zochuluka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena