Genesis 24:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Mwana wa mkaziyo anali wokongola mochititsa kaso,+ ndipo anali namwali amene anali asanagonepo ndi mwamuna.+ Iye analowa m’chitsimemo n’kutunga madzi mumtsuko wake, kenako anatulukamo. Genesis 30:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Rakele anakhala ndi pakati n’kubereka mwana wamwamuna. Ndiyeno iye anati: “Mulungu wandichotsera chitonzo.”+ Rute 4:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Zitatero akazi anayamba kuuza+ Naomi kuti: “Adalitsike Yehova,+ amene wachititsa kuti usasowe wokuwombola lero, kuti dzina lake lifalitsidwe mu Isiraeli. 1 Samueli 1:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Mkazi mnzake wa Hana anali kum’sautsa+ kwambiri n’cholinga choti amukhumudwitse, chifukwa chakuti Yehova anali atatseka mimba yake.
16 Mwana wa mkaziyo anali wokongola mochititsa kaso,+ ndipo anali namwali amene anali asanagonepo ndi mwamuna.+ Iye analowa m’chitsimemo n’kutunga madzi mumtsuko wake, kenako anatulukamo.
23 Rakele anakhala ndi pakati n’kubereka mwana wamwamuna. Ndiyeno iye anati: “Mulungu wandichotsera chitonzo.”+
14 Zitatero akazi anayamba kuuza+ Naomi kuti: “Adalitsike Yehova,+ amene wachititsa kuti usasowe wokuwombola lero, kuti dzina lake lifalitsidwe mu Isiraeli.
6 Mkazi mnzake wa Hana anali kum’sautsa+ kwambiri n’cholinga choti amukhumudwitse, chifukwa chakuti Yehova anali atatseka mimba yake.