Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 15:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Atamaliza kulankhula zimenezi, nthawi yomweyo anataya fupa lija ndi kutcha malowo kuti Ramati-lehi.*+

  • Oweruza 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Chotero Mulungu anang’amba nthaka ku Lehi ndipo madzi+ anayamba kutuluka panthakapo. Pamenepo Samisoni anamwa madziwo, moti anapezanso mphamvu+ ndi kutsitsimulidwa.+ N’chifukwa chake anatcha malowo kuti Eni-hakore.* Malo amenewa ali ku Lehi kufikira lero.

  • 2 Samueli 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Womutsatira anali Shama, mwana wamwamuna wa Age Mharari.+ Tsopano Afilisiti anasonkhana pamodzi ku Lehi, kumene kunali munda wodzaza ndi mphodza.+ Kumeneko anthu anali atathawa chifukwa choopa Afilisitiwo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena