Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kodi okalamba si paja amakhala ndi nzeru,+

      Ndipo amene akhala masiku ambiri si paja amamvetsa zinthu?

  • Miyambo 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Njira ya munthu wopusa imakhala yolondola m’maso mwake,+ koma womvera malangizo ndi wanzeru.+

  • 1 Akorinto 15:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Musasocheretsedwe. Kugwirizana ndi anthu oipa kumawononga makhalidwe abwino.+

  • Tito 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chimodzimodzinso akazi achikulire.+ Akhale ndi khalidwe loyenera anthu opembedza. Asakhale amiseche,+ kapena akapolo a vinyo wambiri, koma akhale aphunzitsi a zinthu zabwino,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena