Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Akatero anali kupisa mumphika kapena chophikira cha zigwiriro ziwiri, munkhali, kapena m’chophikira cha chigwiriro chimodzi. Ndipo wansembe anali kutenga chilichonse chimene folokoyo yatulutsa. Umu ndi mmene anali kuchitira ku Silo, kwa Aisiraeli onse opita kumeneko.+

  • 1 Samueli 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tchimo la atumikiwa linakula kwambiri pamaso pa Yehova,+ chifukwa amuna amenewa sanali kulemekeza nsembe ya Yehova.+

  • 1 Timoteyo 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu amene ali ndi chizolowezi chochita tchimo,+ uwadzudzule+ pamaso pa onse kuti ena onse akhale ndi mantha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena