Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Simunandipereke m’manja mwa adani.+

      Mwapondetsa phazi langa pamalo otakasuka.+

  • Salimo 62:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iye ndiye thanthwe langa ndi chipulumutso changa, malo anga okwezeka ndiponso achitetezo.+

      Sindidzagwedezeka kwambiri.+

  • Salimo 94:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova amadziwa kuti maganizo a anthu ali ngati mpweya wotuluka m’mphuno.+

  • Salimo 118:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kuthawira kwa Yehova n’kwabwino+

      Kusiyana ndi kudalira munthu wochokera kufumbi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena