Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 18:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Apanso Sauli anachita mantha kwambiri ndi Davide, moti anali kudana ndi Davide nthawi zonse.+

  • 1 Samueli 20:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Atatero, Sauli anaponya mkondo wake kuti amulase.+ Pamenepo Yonatani anadziwa kuti bambo ake anatsimikiza mtima kupha Davide.+

  • Salimo 112:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Woipa adzaona zimenezi ndipo adzasautsika.+

      ש [Shin]

      Adzakukuta mano ndi kusungunuka.+

      ת [Taw]

      Chikhumbo cha anthu oipa chidzatha.+

  • Miyambo 11:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Zolakalaka za anthu olungama, ndithu n’zabwino.+ Chiyembekezo cha oipa chimabweretsa mkwiyo woopsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena