Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Zikilaga,+ Beti-marikaboti, Hazara-susa,+

  • 1 Samueli 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno zimene zinachitika n’zakuti, pamene Davide ndi asilikali ake anali kubwerera ku Zikilaga+ tsiku lachitatu, Aamaleki+ anaukira anthu a kum’mwera* ndi a mumzinda wa Zikilaga ndi kufunkha zinthu zawo. Iwo anathira nkhondo mzindawo ndi kuutentha ndi moto.

  • 2 Samueli 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Sauli atamwalira, ndiponso Davide atabwera kuchokera kokakantha Aamaleki,+ Davideyo anakhala ku Zikilaga+ masiku awiri.

  • 1 Mbiri 4:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 ku Betuele,+ ku Horima,+ ku Zikilaga,+

  • 1 Mbiri 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsopano nawa anthu amene anapita kwa Davide ku Zikilaga,+ pa nthawi imene iye sanali kuyenda momasuka chifukwa choopa Sauli+ mwana wa Kisi. Iwowa anali ena mwa amuna amphamvu+ amene anamuthandiza pankhondo.

  • 1 Mbiri 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Davide atapita ku Zikilaga,+ anthu ena a fuko la Manase anapita kumbali yake. Anthuwo anali Adinala, Yozabadi, Yediyaeli, Mikayeli, Yozabadi, Elihu, ndi Ziletai. Aliyense wa amenewa anali mtsogoleri+ wa asilikali 1,000, a fuko la Manase.

  • Nehemiya 11:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 ku Zikilaga,+ ku Mekona ndi midzi yake yozungulira,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena