Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 N’chifukwa chake ndalumbirira a m’nyumba ya Eli kuti mpaka kalekale sadzapewa chilango chifukwa cha cholakwa cha anthu a m’nyumba yakewo, ngakhale atapereka nsembe.”+

  • 1 Samueli 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngakhalenso likasa la Mulungu linalandidwa,+ ndipo Hofeni ndi Pinihasi, ana awiri a Eli, anafa.+

  • 1 Samueli 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno mwamunayo atangotchula za likasa la Mulungu woona, Eli anagwa chagada kuchoka pampando, ali pachipatapo. Chotero khosi lake linathyoka ndipo anafa, pakuti anali wokalamba ndi wonenepa kwambiri. Eli anali ataweruza Isiraeli zaka 40.

  • 1 Samueli 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 (Ahiya ndiye anali kunyamula efodi.+ Iye anali mwana wa Ahitubu,+ m’bale wa Ikabodi,+ mwana wa Pinihasi,+ mwana wa Eli,+ wansembe wa Yehova ku Silo.)+ Koma anthu sanadziwe kuti Yonatani wachoka.

  • 1 Samueli 22:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamapeto pake mfumu inauza Doegi+ kuti: “Iwe, tembenuka ukanthe ansembewa!” Nthawi yomweyo Doegi, Mwedomu,+ anatembenuka n’kukantha ndi kupha+ ansembewo tsiku limenelo, amuna 85 ovala efodi+ wa nsalu.

  • 1 Mafumu 2:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Choncho Solomo anathamangitsa Abiyatara n’kumusiyitsa kutumikira monga wansembe wa Yehova, pokwaniritsa mawu amene Yehova analankhula ku Silo,+ otsutsana ndi nyumba ya Eli.+

  • 1 Mbiri 24:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Davide ndi Zadoki,+ yemwe anali wochokera mwa ana a Eleazara, ndiponso Ahimeleki,+ wochokera mwa ana a Itamara, anagawa ana a Aroniwo m’magulu a udindo pa utumiki wawo.+

  • Salimo 37:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti manja a anthu oipa adzathyoledwa,+

      Koma Yehova adzathandiza anthu olungama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena