1 Samueli 14:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Choncho Yonatani anauza mtumiki wake womunyamulira zida uja kuti: “Tiye tiwolokere kumudzi wa amuna osadulidwawa.+ Pakuti mwina Yehova adzatithandiza, chifukwa palibe chimene chingalepheretse Yehova kupulumutsa anthu ake pogwiritsa ntchito anthu ambiri kapena ochepa.”+ 1 Samueli 17:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Ndiyeno Davide anayamba kufunsa amuna amene anali ataimirira pafupi naye kuti: “Kodi munthu amene angakaphe Mfilisiti+ ameneyu ndi kuchotsa chitonzo pa Isiraeli+ amuchitira chiyani? Kodi Mfilisiti wosadulidwa+ ameneyu ndani kuti azinyoza+ asilikali a Mulungu wamoyo?”+ 2 Samueli 1:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Anthu inu musanene zimenezi mumzinda wa Gati.+Musalengeze zimenezi m’misewu ya Asikeloni,+Kuopera kuti ana aakazi a Afilisiti angasangalale,+Kuopera kuti ana aakazi a anthu osadulidwa angakondwere. Ezekieli 44:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mumatenga alendo osachita mdulidwe wa mtima ndi mdulidwe wa khungu lawo+ kuti alowe m’malo anga opatulika ndi kuwadetsa. Ndithu iwo amadetsa nyumba yanga. Pamene mukupereka chakudya+ changa chomwe ndi mafuta+ ndi magazi,+ pangano langa limaphwanyidwa chifukwa cha zonyansa zanu zonse.+
6 Choncho Yonatani anauza mtumiki wake womunyamulira zida uja kuti: “Tiye tiwolokere kumudzi wa amuna osadulidwawa.+ Pakuti mwina Yehova adzatithandiza, chifukwa palibe chimene chingalepheretse Yehova kupulumutsa anthu ake pogwiritsa ntchito anthu ambiri kapena ochepa.”+
26 Ndiyeno Davide anayamba kufunsa amuna amene anali ataimirira pafupi naye kuti: “Kodi munthu amene angakaphe Mfilisiti+ ameneyu ndi kuchotsa chitonzo pa Isiraeli+ amuchitira chiyani? Kodi Mfilisiti wosadulidwa+ ameneyu ndani kuti azinyoza+ asilikali a Mulungu wamoyo?”+
20 Anthu inu musanene zimenezi mumzinda wa Gati.+Musalengeze zimenezi m’misewu ya Asikeloni,+Kuopera kuti ana aakazi a Afilisiti angasangalale,+Kuopera kuti ana aakazi a anthu osadulidwa angakondwere.
7 Mumatenga alendo osachita mdulidwe wa mtima ndi mdulidwe wa khungu lawo+ kuti alowe m’malo anga opatulika ndi kuwadetsa. Ndithu iwo amadetsa nyumba yanga. Pamene mukupereka chakudya+ changa chomwe ndi mafuta+ ndi magazi,+ pangano langa limaphwanyidwa chifukwa cha zonyansa zanu zonse.+