Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Chifukwa mawu anga ndithu si onama.

      Wodziwa bwino zinthu kwambiri+ ali ndi inu.

  • Yobu 37:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi mukudziwa mmene mtambo umaimira,+

      Ndiponso ntchito zodabwitsa za yemwe amadziwa zinthu bwino kwambiri?+

  • Salimo 147:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ambuye wathu ndi wamkulu ndipo ali ndi mphamvu zochuluka.+

      Nzeru zake zilibe malire.+

  • Aroma 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndithudi, madalitso amene Mulungu amapereka ndi ochuluka kwambiri.+ Nzeru+ zake n’zozama, ndiponso iye ndi wodziwa zinthu kwambiri.+ Ziweruzo zake ndi zosasanthulika,+ ndipo ndani angatulukire njira zake?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena