Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Dzanja lanu lamanja, inu Yehova, likusonyeza kupambana kwa mphamvu zake.+

      Dzanja lanu lamanja, inu Yehova, limaphwanya mdani.+

  • Salimo 21:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dzanja lanu lidzapeza adani anu onse.+

      Dzanja lanu lamanja lidzapeza odana nanu.

  • Salimo 92:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti taonani adani anu, inu Yehova!+

      Adani anu onse adzatha!+

      Anthu onse ochita zopweteka anzawo adzamwazikana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena