Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Choncho anthu inu munayandikira ndi kuimirira m’munsi mwa phiri. Phiri limenelo linali kuyaka moto mpaka kumwamba, ndipo kunali mdima ndi mtambo wakuda.+

  • 1 Mafumu 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa nthawi imeneyo Solomo anati: “Yehova anati adzakhala mu mdima wandiweyani.+

  • Salimo 18:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye anaweramitsa kumwamba n’kutsika.+

      Mdima wandiweyani unali kunsi kwa mapazi ake.

  • Salimo 97:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mitambo ndi mdima wandiweyani zamuzungulira.+

      Chilungamo ndi chiweruzo ndizo malo okhazikika a mpando wake wachifumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena