2 Samueli 18:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Choncho mfumu inawauza kuti: “Ndichita zilizonse zimene inu mukuona kuti n’zabwino.”+ Pamenepo mfumu inangoima pambali pa chipata,+ ndipo anthu onse anapita kunkhondo m’magulu a anthu 100 ndi 1,000.+ 2 Samueli 18:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Tsopano Davide anali atakhala pakati pa zipata ziwiri.+ Pa nthawiyi mlonda+ anakwera padenga la mpanda kuchipata. Ndiyeno atakweza maso anaona munthu akuthamanga ali yekha. 1 Mafumu 22:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Mfumu ya Isiraeli ndi Yehosafati mfumu ya Yuda anali atakhala pabwalo* la pachipata cha Samariya. Aliyense anakhala pampando wake wachifumu atavala zovala zachifumu.+ Pamaso pawo panali aneneri onse ndipo anali kuchita zinthu monga mmene aneneri amachitira.+ Yeremiya 38:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Tsopano Ebedi-meleki Mwitiyopiya,*+ amene anali nduna m’nyumba ya mfumu, ndipo pa nthawiyo anali m’nyumbamo, anamva kuti Yeremiya amuponya m’chitsime. Apa n’kuti mfumu itakhala pansi ku Chipata cha Benjamini.+
4 Choncho mfumu inawauza kuti: “Ndichita zilizonse zimene inu mukuona kuti n’zabwino.”+ Pamenepo mfumu inangoima pambali pa chipata,+ ndipo anthu onse anapita kunkhondo m’magulu a anthu 100 ndi 1,000.+
24 Tsopano Davide anali atakhala pakati pa zipata ziwiri.+ Pa nthawiyi mlonda+ anakwera padenga la mpanda kuchipata. Ndiyeno atakweza maso anaona munthu akuthamanga ali yekha.
10 Mfumu ya Isiraeli ndi Yehosafati mfumu ya Yuda anali atakhala pabwalo* la pachipata cha Samariya. Aliyense anakhala pampando wake wachifumu atavala zovala zachifumu.+ Pamaso pawo panali aneneri onse ndipo anali kuchita zinthu monga mmene aneneri amachitira.+
7 Tsopano Ebedi-meleki Mwitiyopiya,*+ amene anali nduna m’nyumba ya mfumu, ndipo pa nthawiyo anali m’nyumbamo, anamva kuti Yeremiya amuponya m’chitsime. Apa n’kuti mfumu itakhala pansi ku Chipata cha Benjamini.+