Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ngati ndikanati sindikuopa kusautsidwa ndi mdani,+

      Kuti adani awo angamve molakwa,+

      Kutinso anganene kuti: “Dzanja lathu lapambana,+

      Ndipo si Yehova amene wachita zonsezi.”+

  • Salimo 58:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wolungama adzasangalala chifukwa chakuti waona oipa akupatsidwa chilango.+

      Adzasambitsa mapazi ake m’magazi a anthu oipa.+

  • Ezekieli 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma ine ndinachita zinthu molemekeza dzina langa kuti lisadetsedwe pamaso pa anthu a mitundu ina amene iwo anali kukhala pakati pawo,+ pakuti ndinawachititsa kuti andidziwe pamaso pa anthu a mitundu inawo powatulutsa m’dziko la Iguputo.+

  • Ezekieli 36:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Chotero uza nyumba ya Isiraeli kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Sindidzachita zimenezi chifukwa cha inuyo a nyumba ya Isiraeli, koma chifukwa cha dzina langa loyera limene mwalidetsa pakati pa anthu a mitundu ina kumene munapita.”’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena