-
2 Mbiri 18:31Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
31 Akuluakulu oyang’anira asilikali okwera magaleta aja atangomuona Yehosafati, anaganiza kuti: “Iyi ndiyo mfumu ya Isiraeli.”+ Choncho anatembenuka kuti amenyane naye, koma Yehosafati anayamba kukuwa popempha thandizo,+ ndipo Yehova anamuthandiza.+ Nthawi yomweyo Mulungu anawachititsa kuchoka kwa iye.+
-