Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Atatero, Yehonadabu anamuuza kuti: “Ugone pabedi lako ndi kunamizira kudwala.+ Mosakayikira bambo ako adzabwera kudzakuona, ndipo udzawauze kuti, ‘Chonde lolani kuti mlongo wanga Tamara abwere adzandipatse chakudya monga munthu wodwala. Ndikufuna kuti andipangire chakudya chonditonthoza pamaso panga, ine ndikuona, ndipo ndidye kuchokera m’manja mwake.’”+

  • 1 Mafumu 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zitatero, Bati-seba analowa kuchipinda kumene kunali mfumu.+ Mfumuyo inali yokalamba+ kwambiri ndipo Abisagi+ Msunemu anali kuisamalira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena