Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 “Tsopano inu Yehova Mulungu, chitani mpaka kalekale mawu amene mwalankhula okhudza mtumiki wanu ndi nyumba yake. Chitani mmene mwanenera.+

  • 1 Mbiri 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzamukhazikitsa iye kukhala woyang’anira nyumba yanga+ ndi ufumu wanga+ mpaka kalekale, ndipo mpando wake wachifumu+ sudzatha mpaka kalekale.”’”

  • 2 Mbiri 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano inu Yehova Mulungu, kwaniritsani+ lonjezo limene munapereka kwa Davide bambo anga. Pakuti ndinu amene mwandiika kukhala mfumu+ ya anthuwa amene ndi ochuluka kwambiri ngati fumbi lapadziko lapansi.+

  • Salimo 119:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  49 Kumbukirani mawu amene munandiuza ine mtumiki wanu,+

      Mawu amene ndikuwayembekezera malinga ndi lonjezo lanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena