Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Inuyo mudzakhala ufumu wanga wa ansembe ndi mtundu wanga woyera.’+ Ukanene mawu amenewa kwa ana a Isiraeli.”

  • Numeri 23:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti pomwe ndili pano ndikutha kuwaona, pamwamba pa matanthwe pano,

      Ndikuwaona ndithu, pano pamwamba pa mapiri.

      Akukhala paokhaokha m’mahema awo,+

      Iwo akudziona kuti ndi osiyana ndi mitundu ina.+

  • Deuteronomo 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kapena kodi Mulungu anayamba wapitapo kukadzitengera mtundu wa anthu pakati pa mtundu wina ndi mayesero,+ zizindikiro,+ zozizwitsa,+ nkhondo,+ dzanja lamphamvu,+ mkono wotambasula,+ ndi zoopsa zazikulu+ zofanana ndi zimene Yehova Mulungu wanu anakuchitirani ku Iguputo inu mukuona?

  • Deuteronomo 32:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti gawo la Yehova ndilo anthu ake.+

      Yakobo ndiye gawo la cholowa chake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena