Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepo Hana anaimirira atadya ndi kumwa ku Silo. Apa n’kuti Eli wansembe atakhala pampando, pakhomo la kachisi+ wa Yehova.

  • Nehemiya 10:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Wansembe, mwana wamwamuna wa Aroni, azikhala ndi Alevi pamene iwo akulandira chakhumi.* Aleviwo azipereka gawo limodzi mwa magawo 10 a chakhumicho kunyumba ya Mulungu+ wathu kuzipinda zodyera+ m’nyumba yosungiramo zinthu.

  • Yeremiya 35:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Pita kunyumba ya Arekabu,+ ndipo ukalankhule nawo ndi kubwera nawo kunyumba ya Yehova. Ukalowe nawo m’chimodzi mwa zipinda zodyera ndipo ukawapatse vinyo kuti amwe.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena