Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chiritsani odwala,+ ukitsani anthu akufa, yeretsani akhate, tulutsani ziwanda. Munalandira kwaulere, patsani kwaulere.+

  • 1 Akorinto 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho mphoto yanga ndi chiyani? Ndi yakuti polengeza uthenga wabwino ndipereke uthengawo kwaulere,+ kuti ndisagwiritse ntchito molakwa ufulu wanga pa zinthu zokhudzana ndi uthenga wabwino.

  • 2 Akorinto 11:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma pamene ndinasowa zofunika zina ndili kwanuko, sindinalemetse ngakhale munthu mmodzi,+ popeza abale amene anachokera ku Makedoniya+ anandipatsa zonse zimene ndinali kuzisowa. Ndithu, sindinakulemetseni m’njira iliyonse, ndipo ndipitirizabe kutero.+

  • Chivumbulutso 22:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mzimu+ ndi mkwatibwi+ akunenabe kuti: “Bwera!” Aliyense wakumva anene kuti: “Bwera!”+ Aliyense wakumva ludzu abwere.+ Aliyense amene akufuna, amwe madzi a moyo kwaulere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena