Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako Davide anati: “Mwana wanga Solomo ndi wamng’ono komanso wosakhwima,+ koma nyumba yoti adzamangire Yehova idzakhala yokongola,+ yaulemerero wosaneneka+ ndiponso yotchuka ndi yotamandika kumayiko onse. Ndiyetu ndim’konzere zipangizo zoti adzagwiritsire ntchito.” Chotero Davide asanafe, anasonkhanitsa zipangizo zambirimbiri pokonzekera ntchitoyo.+

  • 1 Mbiri 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Golide, siliva, mkuwa, ndi zitsulo n’zosatheka kuziwerenga.+ Yamba kugwira ntchito imeneyi,+ ndipo Yehova akhale nawe.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena