Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwo anayamba kusonkhana kwa ine, aliyense akunjenjemera+ chifukwa cha mawu a Mulungu wa Isiraeli otsutsa kusakhulupirika kwa anthu amene anabwerera kuchokera ku ukapolo. Pa nthawiyi n’kuti ine nditakhala pansi ndili wokhumudwa ndi wachisoni kwambiri, ndipo ndinakhala choncho mpaka nthawi yopereka nsembe yambewu yamadzulo.+

  • Danieli 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndinayang’ana+ kwa Yehova Mulungu woona kuti ndimufunefune mwa kupemphera,+ kumuchonderera, kusala kudya, kuvala ziguduli* ndi kudzithira phulusa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena