Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 59:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inu Yehova, Mulungu wa makamu, ndinu Mulungu wa Isiraeli.+

      Nyamukani ndi kuweruza mitundu yonse ya anthu.+

      Musakomere mtima aliyense woipa ndi wachiwembu.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 69:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Wonjezerani zolakwa pa zolakwa zawo,+

      Ndipo inu musawaone monga olungama.+

  • Yeremiya 18:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma inu Yehova mukudziwa bwino chiwembu chimene andikonzera kuti andiphe.+ Musakhululukire* cholakwa chawo, ndipo musafafanize tchimo lawolo pamaso panu. Koma iwo apunthwe pamaso panu.+ Muwachitire zimenezi pa nthawi ya mkwiyo wanu.+

  • 2 Timoteyo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Alekizanda,+ wosula zinthu zamkuwa uja, anandichitira zoipa zambiri. Yehova adzamubwezera malinga ndi ntchito zake,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena