Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 35:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Amene akufunafuna moyo wanga achite manyazi ndi kunyozeka.+

      Amene akundikonzera chiwembu muwabweze ndipo athedwe nzeru.+

  • Salimo 59:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inu Yehova, Mulungu wa makamu, ndinu Mulungu wa Isiraeli.+

      Nyamukani ndi kuweruza mitundu yonse ya anthu.+

      Musakomere mtima aliyense woipa ndi wachiwembu.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 109:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Yehova akumbukire cholakwa cha makolo ake,+

      Ndipo tchimo la mayi ake+ lisafafanizidwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena