3 Pa nthawi imeneyo Tatenai+ bwanamkubwa wa kutsidya lina la Mtsinje,*+ Setara-bozenai, ndi anzawo anabwera kwa Ayudawo n’kudzawafunsa kuti: “Kodi ndani wakulamulani kuti mumange nyumbayi ndi kumaliza khoma* lamatabwali?”+
7 Kenako Melatiya Mgibeoni+ ndi Yadoni Mmeronoti+ anakonza mpandawo kuchokera pamene Yoyada ndi Mesulamu analekezera. Amenewa anali amuna a ku Gibeoni+ ndi Mizipa+ amene anali pansi pa ulamuliro wa bwanamkubwa+ wa kutsidya la Mtsinje.+