Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Thyolani dzanja la woipa ndi wankhanzayo.+

      Fufuzani zoipa zake zonse ndi kumulanga kufikira zoipazo zitatha.+

  • Yeremiya 48:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 “‘Nyanga* ya Mowabu yadulidwa+ ndipo dzanja lake lathyoledwa,’+ watero Yehova.

  • Ezekieli 30:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ine ndithana ndi Farao mfumu ya Iguputo.+ Ndidzathyola manja ake onse,+ dzanja lamphamvu ndi lothyoka lija,+ ndipo ndidzachititsa kuti lupanga ligwe m’dzanja lake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena