Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 41:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 “Kodi ungawedze ng’ona*+ ndi mbedza?

      Kapena ungamange lilime lake ndi chingwe?

  • Yobu 41:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Palibe angalimbe mtima kuti aipute.

      Kodi ndani angaimitsane nane?+

  • Salimo 74:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Inu munaphwanya mitu ya Leviyatani*+ kukhala zidutswazidutswa.

      Munaipereka kwa anthu monga chakudya, munaipereka kwa anthu okhala m’madera opanda madzi.+

  • Salimo 104:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Zombo zimayenda mmenemo.+

      Ndipo Leviyatani*+ munam’panga kuti azisewera mmenemo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena