Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mfumuyo inalumbira+ kuti: “Pali Yehova+ amene anapulumutsa+ moyo wanga+ m’masautso onse,+

  • Salimo 71:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndikafuna kuimba nyimbo zokutamandani, pakamwa panga padzafuula mokondwera,+

      Ngakhalenso moyo wanga umene mwauwombola+ udzakutamandani.

  • Salimo 103:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Tamanda amene akuwombola moyo wako kudzenje,+

      Amene akukuveka kukoma mtima kosatha ndi chifundo ngati chisoti chachifumu,+

  • Maliro 3:58
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 58 Inu Yehova, mwandiweruzira milandu yanga.+ Mwawombola moyo wanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena