Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 37:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Wamphamvuyonse sitikumudziwa.+

      Iye ali ndi mphamvu zambiri,+

      Ndipo sadzanyoza+ chilungamo+ ndi kulungama kochuluka.+

  • Salimo 11:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pakuti Yehova ndi wolungama.+ Amakonda ntchito zolungama.+

      Anthu owongoka mtima ndi amene adzaona nkhope yake.+

  • Salimo 33:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Iye amakonda chilungamo ndi chiweruzo chosakondera.+

      Dziko lapansi ladzaza ndi kukoma mtima kosatha kwa Yehova.+

  • Yeremiya 9:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Koma amene akudzitamanda adzitamande pa chifukwa chakuti, amamvetsa bwino+ njira zanga ndipo amandidziwa, kuti ine ndine Yehova,+ amene ndimasonyeza kukoma mtima kosatha, ndimapereka ziweruzo ndi kuchita chilungamo padziko lapansi.+ Pakuti zinthu zimenezi zimandisangalatsa,”+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena