-
Salimo 105:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Kumbukirani ntchito zodabwitsa zimene wachita,+
Kumbukirani zozizwitsa zake ndi zigamulo zotuluka m’kamwa mwake,+
-
Yesaya 63:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Ndidzanena za ntchito za Yehova zosonyeza kukoma mtima kwake kosatha.+ Ndidzatamanda Yehova, mogwirizana ndi zonse zimene Yehova watichitira.+ Ndidzauza nyumba ya Isiraeli zabwino zochuluka+ zimene iye wawachitira chifukwa cha chifundo chake,+ komanso chifukwa cha kukoma mtima kwake kosatha ndiponso kwakukulu.
-
-
-