Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa cha mtambowo, ansembewo+ analephera kupitiriza kutumikira,+ popeza ulemerero+ wa Yehova unadzaza nyumba ya Yehovayo.+

  • Salimo 57:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inu Mulungu, kwezekani kupitirira kumwamba.+

      Ulemerero wanu ukhale pamwamba pa dziko lonse lapansi.+

  • Salimo 104:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ulemerero wa Yehova udzakhalapobe mpaka kalekale.+

      Yehova adzakondwera ndi ntchito zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena