Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ali pabedi lake amakonza chiwembu kuti apweteke anzake.+

      Amaima panjira yoipa.+

      Sapewa kuchita zinthu zoipa.+

  • Salimo 64:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Amafunafuna kuchita zinthu zosalungama,+

      Abisa chiwembu chimene achikonza mochenjera,+

      Ndipo zamkati, zamumtima mwa aliyense, n’zovuta kuzimvetsa.+

  • Miyambo 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 mtima wokonzera ena ziwembu,+ mapazi othamangira kukachita zoipa,+

  • Zekariya 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Musamabere mwachinyengo mkazi wamasiye,+ mwana wamasiye,*+ mlendo+ kapena munthu wosautsika.+ Musamakonzerane chiwembu mumtima mwanu.’+

  • Mateyu 5:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Koma ine ndikukuuzani kuti aliyense woyang’anitsitsa mkazi+ mpaka kumulakalaka, wachita naye kale chigololo+ mumtima mwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena