Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mudzandiwonjola mu ukonde umene anditchera,+

      Pakuti inu ndinu malo anga achitetezo.+

  • Salimo 91:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti iye adzakupulumutsa mumsampha wa wosaka mbalame,+

      Ndi ku mliri wobweretsa masautso.+

  • Salimo 124:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Moyo wathu uli ngati mbalame imene yathawa+

      Pamsampha wa munthu wogwiritsa ntchito nyambo.+

      Msamphawo wathyoka,+

      Ndipo ife tapulumuka.+

  • 2 Timoteyo 2:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Komanso kuti mwina nzeru zawo zingabwereremo kuti awonjoke mumsampha+ wa Mdyerekezi, poona kuti wawagwira amoyo+ pofuna kukwaniritsa cholinga chake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena