2 Samueli 3:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Pamenepo Yowabu anapita kwa mfumu n’kunena kuti: “N’chiyani chimene mwachitachi?+ Abineri anabwera kwa inu. N’chifukwa chiyani mwamulola kuti anyamuke ndi kupita mwamtendere? 2 Samueli 3:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Ine lero ndafooka ngakhale kuti ndine mfumu yodzozedwa,+ ndipo ine ndikuona kuti amuna awa, ana a Zeruya,+ achita nkhanza kwambiri.+ Yehova abwezere aliyense wochita zinthu zoipa mogwirizana ndi kuipa kwake.”+ Mlaliki 10:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ndaonapo antchito atakwera pamahatchi,* koma akalonga akuyenda pansi ngati antchito.+ Yesaya 3:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Anthu azidzalamulirana mwankhanza, ndipo munthu azidzachitira nkhanza munthu mnzake.+ Mnyamata adzaukira nkhalamba,+ ndipo wonyozeka adzaukira wolemekezeka.+
24 Pamenepo Yowabu anapita kwa mfumu n’kunena kuti: “N’chiyani chimene mwachitachi?+ Abineri anabwera kwa inu. N’chifukwa chiyani mwamulola kuti anyamuke ndi kupita mwamtendere?
39 Ine lero ndafooka ngakhale kuti ndine mfumu yodzozedwa,+ ndipo ine ndikuona kuti amuna awa, ana a Zeruya,+ achita nkhanza kwambiri.+ Yehova abwezere aliyense wochita zinthu zoipa mogwirizana ndi kuipa kwake.”+
5 Anthu azidzalamulirana mwankhanza, ndipo munthu azidzachitira nkhanza munthu mnzake.+ Mnyamata adzaukira nkhalamba,+ ndipo wonyozeka adzaukira wolemekezeka.+