Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 4:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ankalankhula miyambi 3,000+ ndipo nyimbo zake+ zinakwana 1,005.

  • Miyambo 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Miyambi+ ya Solomo+ mwana wa Davide,+ mfumu ya Isiraeli,+

  • Miyambo 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Miyambi ya Solomo.+

      Mwana wanzeru amakondweretsa bambo ake,+ koma mwana wopusa amamvetsa chisoni mayi ake.+

  • Mlaliki 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kuwonjezera pa kukhala ndi nzeru,+ wosonkhanitsayo nthawi zonse anali kuphunzitsanso anthuwo kuti adziwe zinthu.+ Anali kusinkhasinkha ndi kufufuza zinthu mosamala,+ ndipo analemba miyambi yambiri m’ndondomeko yoyenera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena