Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Madalitso onsewa adzakutsata ndi kukupeza+ chifukwa ukumvera mawu a Yehova Mulungu wako:

  • Yobu 42:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova anadalitsa+ kwambiri mapeto a Yobu kuposa chiyambi chake+ moti iye anakhala ndi nkhosa 14,000, ngamila 6,000, ng’ombe 2,000 zimene zinkagwira ntchito zili ziwiriziwiri, ndi abulu aakazi 1,000.

  • Salimo 37:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndinali mwana, ndipo tsopano ndakula,+

      Koma sindinaonepo munthu aliyense wolungama atasiyidwa,+

      Kapena ana ake akupemphapempha chakudya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena