Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 26:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti kukoma mtima kwanu kosatha kuli pamaso panga.

      Ine ndayenda m’choonadi chanu.+

  • Miyambo 10:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chuma cha anthu oipa chidzakhala chopanda phindu,+ koma chilungamo n’chimene chidzapulumutse munthu ku imfa.+

  • Miyambo 13:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Chilungamo chimateteza munthu amene sachita zopweteka ena,+ koma wochimwa amawonongedwa ndi zoipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena