Mlaliki 12:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Wosonkhanitsayo anafufuza mawu okoma+ ndipo analemba mawu olondola a choonadi.+ Luka 4:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Pamenepo onse anayamba kumutamanda ndi kudabwa ndi mawu ogwira mtima+ otuluka pakamwa pake, mwakuti anali kunena kuti: “Kodi iyeyu si mwana wa Yosefe?”+ 2 Akorinto 5:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Choncho popeza timaopa+ Ambuye, tikupitiriza kukopa+ anthu. Mulungu akudziwa bwino zolinga zathu. Koma ndili ndi chikhulupiriro kuti inunso, mwachikumbumtima chanu, mukudziwa bwino zolinga zathu.+ Akolose 4:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Nthawi zonse mawu anu azikhala achisomo,+ okoma ngati kuti mwawathira mchere,+ kuti mudziwe mmene mungayankhire+ wina aliyense.
22 Pamenepo onse anayamba kumutamanda ndi kudabwa ndi mawu ogwira mtima+ otuluka pakamwa pake, mwakuti anali kunena kuti: “Kodi iyeyu si mwana wa Yosefe?”+
11 Choncho popeza timaopa+ Ambuye, tikupitiriza kukopa+ anthu. Mulungu akudziwa bwino zolinga zathu. Koma ndili ndi chikhulupiriro kuti inunso, mwachikumbumtima chanu, mukudziwa bwino zolinga zathu.+
6 Nthawi zonse mawu anu azikhala achisomo,+ okoma ngati kuti mwawathira mchere,+ kuti mudziwe mmene mungayankhire+ wina aliyense.