Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 76:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu ndinu wochititsa mantha,+

      Ndani angaime pamaso panu inu mutakwiya kwambiri?+

  • Yesaya 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Lowani muthanthwe ndipo dzibiseni m’fumbi chifukwa cha kuopsa kwa Yehova, ndiponso chifukwa cha ulemerero ndi ukulu wake.+

  • Luka 23:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 M’masiku amenewo iwo adzayamba kuuza mapiri kuti, ‘Tigwereni!’ ndipo adzauza zitunda kuti, ‘Tikwirireni!’+

  • 2 Atesalonika 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Amenewa adzawaweruza kuti alandire chilango+ cha chiwonongeko chamuyaya,+ kuwachotsa pamaso pa Ambuye ndi ku ulemerero wa mphamvu zake.+

  • Chivumbulutso 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mafumu a dziko lapansi, nduna, akuluakulu a asilikali, olemera, amphamvu, kapolo aliyense ndi mfulu aliyense, anabisala m’mapanga ndi m’matanthwe+ a m’mapiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena