21 Anthu ako onse adzakhala olungama.+ Iwo adzakhala m’dzikomo mpaka kalekale.+ Anthuwo adzakhala mmera wobzalidwa ndi ine+ ndiponso ntchito ya manja anga,+ kuti ineyo ndikongoletsedwe.+
12 Zimenezi zatiphunzitsa kukana moyo wosaopa Mulungu+ ndi zilakolako za dziko,+ koma kukhala amaganizo abwino, achilungamo ndi odzipereka kwa Mulungu+ m’nthawi* ino.+
13 Koma pali kumwamba kwatsopano+ ndi dziko lapansi latsopano+ zimene ife tikuyembekezera mogwirizana ndi lonjezo lake, ndipo mmenemo mudzakhala chilungamo.+